Mawu Amunsi
a Ena polemba mawu a anthu akhungu, amafupikitsako mawu kuti asawononge malo ambili. Mwacitsanzo, m’kalembedwe ka giledi 2 ka anthu akhungu, mawu odziŵika bwino komanso mawu ena amangowalemba mwacidule. Conco, buku la giledi 2 la anthu akhungu n’naling’ono poyelekezela na buku la giledi 1 la anthu akhungu.