LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi
    Nsanja ya Mlonda—2014 | November 15
    • N’zokondweletsa kuti zocitika za pa lemba la Chivumbulutso 11:1, 2 zimagwilizana ndi nthawi pamene kacisi wa kuuzimu anali kudzayezedwa, kapena kupimidwa. Mofananamo, Malaki caputala 3 amachula za kuyendela kacisi wa kuuzimu, ndiyeno pambuyo pake kuuyeletsa. (Mal. 3:1-4) Kodi nchito yoyendela ndi yoyeletsa imeneyo inatenga utali wotani? Nchito imeneyi inayamba mu 1914, mpaka kuciyambi kwa 1919. Nthawi imeneyi imaphatikizapo masiku 1,260 (kapena miyezi 42) ndi masiku atatu ndi hafu ophiphilitsa ochulidwa pa Chivumbulutso caputala 11.

  • Mafunso Ocokela kwa Aŵelengi
    Nsanja ya Mlonda—2014 | November 15
Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani