LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 March tsa. 5
  • Tili ku Mapeto a Dongosolo Lino la Zinthu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tili ku Mapeto a Dongosolo Lino la Zinthu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • “Ufumu Wanu Ubwele”
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
  • Tipita Nanu Limodzi
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • “Tipita Nanu Limodzi”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • ‘Mzimu Umacitila Umboni Limodzi Ndi Mzimu Wathu’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 March tsa. 5
Yesu akamba na Petulo, Andireya, Yakobo, na Yohane

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Tili ku Mapeto a Dongosolo Lino la Zinthu

Tambani vidiyo yakuti Tili ku Mapeto a Dongosolo Lino la Zinthu, ndiyeno yankhani mafunso otsatilawa okhudzana na lemba la Mateyu 24:34.

Chati coonetsa “m’badwo uwu”
  • Kodi mau akuti “zinthu zonsezi” atanthauza ciani?

  • Kodi lemba la Ekisodo 1:6 itithandiza bwanji kumvetsa tanthauzo la mau akuti “m’badwo”?

  • Ni m’badwo uti kweni-kweni umene Yesu anali kukambapo?

  • Ni magulu aŵili ati amene amapanga “m’badwo uwu”?

  • Kodi mau a Yesu aonetsa bwanji kuti tili mkati mweni-mweni mwa masiku otsiliza?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani