LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • Sungani Mgwilizano wa Mpingo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
    • 3. Kodi muyenela kucita ciyani mukasemphana maganizo na Mkhristu mnzanu?

      Ndife ogwilizana inde, koma sitili angwilo. Nthawi zina tingakhumudwitsane kapena kukwiyitsana wina na mnzake. Conco Mawu a Mulungu amatiuza kuti “pitilizani . . . kukhululukilana ndi mtima wonse.” Ndipo amawonjezela kuti: “Monga Yehova anakukhululukilani ndi mtima wonse, inunso teloni.” (Ŵelengani Akolose 3:13) Ngakhale kuti Yehova takhala tikumukwiyitsa maulendo osaŵelengeka, iye amatikhululukilabe. Conco, iye amatiyembekezela kucita cimodzimodzi kwa abale athu. Mukazindikila kuti mwakwiyitsa munthu wina, khalani woyamba kucitapo kanthu kuti muyanjanenso.—Ŵelengani Mateyu 5:23, 24.b

  • Sungani Mgwilizano wa Mpingo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
    • Nthawi zina timakhumudwitsa anthu ena. Zimenezi zikacitika, kodi tiyenela kucita bwanji? Tambani VIDIYO, kenako kambilanani funso lotsatila

      VIDIYO: Kukhazikitsa Mtendele Kumabweletsa Madalitso (6:01)

      • Kodi mlongo wa mu vidiyo iyi anacita ciyani kuti asungitse mtendele?

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani