LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • Mfumu Imveketsa Bwino Mfundo Zokhudza Ufumu wa Mulungu
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
    • 3, 4. (a) Kodi Yesu wakhala akuphunzitsa bwanji anthu okhulupilika za Ufumu wa Mulungu? (b) Kodi tiphunzila ciani m’nkhani ino?

      3 Yesu anakamba mau a pa Yohane 16:12 pausiku wake womaliza padziko lapansi. Kodi zikanatheka bwanji kuti Yesu apitilize kuphunzitsa anthu okhulupilika za Ufumu wa Mulungu pambuyo pa imfa yake? Iye anatsimikizila atumwi ake kuti: “Mzimu wa coonadi, adzakutsogolelani m’coonadi conse.”a (Yoh. 16:13) Mzimu woyela uli ngati munthu wotsogolela amene ndi woleza mtima. Yesu amagwilitsila nchito mzimu kuphunzitsa otsatila ake zinthu zilizonse zimene afunika kudziŵa ponena za Ufumu wa Mulungu panthawi yoyenela.

  • Mfumu Imveketsa Bwino Mfundo Zokhudza Ufumu wa Mulungu
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
    • a Buku lina limanena kuti liu Lacigiriki limene analimasulila kuti ‘kutsogolela’ pa vesili limatanthauza “kusonyeza njila.”

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani