LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • Mafunso Ocokela Kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda (Yophunzila)—2018 | December
    • Nanga “paradaiso” amene Paulo anachula n’ciani?

      Liwu lakuti “paradaiso” lingatanthauze zinthu zosiyana-siyana. Mwacitsanzo, (1) lingatanthauze Paradaiso wakutsogolo wa padziko lapansi, ngati amene Mulungu anaikamo anthu oyambilila. (2) Lingatanthauze umoyo wabwino wauzimu umene anthu a Mulungu adzakhala nawo m’dziko latsopano. (3) Lingatanthauze umoyo wabwino wakumwamba, kapena kuti “paradaiso wa Mulungu” wochulidwa pa Chivumbulutso 2:7.—Onani Nsanja ya Mlonda ya July 15, 2015, peji 8. pala. 8.

      N’kutheka kuti pa 2 Akorinto 12:4, Paulo anali kukamba za maparadaiso onse atatu amenewa pofotokoza zimene zinam’citikila.

  • Mafunso Ocokela Kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda (Yophunzila)—2018 | December
    • “Paradaiso” wa m’masomphenya, amene Paulo ‘anakwatulidwa n’kukalowamo,’ mwacionekele ni (1) Paradaiso weni-weni wa padziko lapansi amene adzakhalapo kutsogolo, (2) paradaiso wauzimu amene adzakhalapo panthawiyo, amene adzakula kwambili kuposa paradaiso wauzimu amene alipo masiku ano, komanso (3) “paradaiso wa Mulungu” wa kumwamba. M’dziko latsopano, maparadaiso onse atatuwa adzakhalapo pa nthawi imodzi.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani