LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • Kodi Baibo Imati Ciyani pa Nkhani ya Umbeta na Ukwati?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
    • 7. Sungani malamulo a Yehova mu ukwati wanu

      Pafunikila khama kuti munthu azitsatila malamulo a Yehova mu ukwati.c Ndipo Yehova amadalitsa amene amayesetsa kutelo. Tambani VIDIYO.

      VIDIYO: Mukhoza Kusunga Malamulo a Yehova a Ukwati (4:14)

      Ŵelengani Aheberi 13:4, na kukambilana mafunso aya:

      • Kodi muganiza n’zotheka kutsatila malamulo a Yehova a mu ukwati? Mwayankha conco cifukwa ciyani?

      Yehova amafuna kuti Akhristu akakwatilana kapena kusudzulana azilembetsa ku boma. M’maiko ambili, izi n’zimene malamulo amafuna. Ŵelengani Tito 3:1, na kukambilana funso ili:

      • Ngati muli pabanja, kodi mukutsimikiza kuti ukwati wanu ni wolembetsa ku boma?

  • Kodi Baibo Imati Ciyani pa Nkhani ya Umbeta na Ukwati?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
    • c Ngati munangotengana cabe na munthu amene simunamange naye ukwati, muyenela kupanga cisankho inu mwini, cokamangitsa naye ukwati kapena kusiyana naye.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani