LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 120
  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mvela Udalitsike
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Ndinu ‘Wokonzeka Kumvela’?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Ni Moyo Wawo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ni Moyo Wawo
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 120

Nyimbo 120

Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso

(Luka 11:28)

1. Kodi ndife anthu omvera Khristu

Pa zonse zimene ananena?

Kuzidziwa n’kosangalatsa ndithu.

Tidalitsidwa tikazimvera.

(KOLASI)

Mvera udalitsidwe

Kuti usangalale.

Zomwe Mulungu angakuuze

Mvera udalitsidwe.

2. Monga nyumba yomangidwa pathanthwe

Osati yomangidwa pamchenga,

Zochita zathu zingatiteteze

Kokha ngati Yesu timumvera.

(KOLASI)

Mvera udalitsidwe

Kuti usangalale.

Zomwe Mulungu angakuuze

Mvera udalitsidwe.

3. Monga mtengo wamumbali mwa madzi

Umabereka nthawi ’kafika,

Tikamvera tidzadalitsidwadi

Moyo wosatha tidzalandira.

(KOLASI)

Mvera udalitsidwe

Kuti usangalale.

Zomwe Mulungu angakuuze

Mvera udalitsidwe.

(Onaninso Deut. 28:2; Sal. 1:3; Miy. 10:22; Mat. 7:24-27.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani