LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 49
  • Yehova Ndi Pothawira Pathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Ndi Pothawira Pathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Ndiye Pothaŵila Pathu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kodi Mumathaŵila kwa Yehova?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Tikhale Okhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 49

Nyimbo 49

Yehova Ndi Pothawira Pathu

(Salmo 91)

1. Yehova m’pothawira

Tidalira iye.

Tikhalebe mumthunzi

Wake, tisachoke.

Iye adzatiteteza,

Tidalire mphamvu zake.

Yehova M’lungu wathu,

Ateteza olungama.

2. Kaya ambiri agwe

Pambali pa iwe,

Udzatetezeka ndi

Okhulupirika.

Sudzaopa ngati kuti

Ndiwe udzawonongedwe

Udzaziona izi,

Uli mumapiko ake.

3. M’lungu akuteteza

Ukamayesedwa.

Sudzafooka ayi

Chifukwa cha mantha.

Sudzaopa mkango, ndipo

Chinjokanso udzaponda.

Yehova m’pothawira,

Amatisamaliradi.

(Onaninso Sal. 97:10; 121:3, 5; Yes. 52:12.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani