LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 84
  • “Ndikufuna”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Ndikufuna”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Nifuna’
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Uziyenda na Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Yendani ndi Mulungu!
    Imbirani Yehova
  • Tifunika Kuphunzitsidwa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 84

Nyimbo 84

“Ndikufuna”

(Luka 5:13)

1. Anasonyeza chikondi

Pobweradi padzikoli.

Mwana wa Mulungu

Kukhala ndithu

Ndi anthu n’kuwaphunzitsa.

Anachiritsa odwala,

Akhungu ndi olumala.

Analitu wokhulupirika

Ananena: “Ndikufuna.”

2. Yehova watithandiza

Chifukwatu watipatsa

Mphatso ya Kapolo.

Tigwira ntchito

Nayetu mosangalala.

Ngati timakonda anthu

Iwo adzadziwiratu.

Choncho amasiye akapempha

Uwauze: “Ndikufuna.”

(Onaninso Yoh. 18:37; Aef. 3:19; Afil. 2:7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani