LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 13
  • Pemphero Loyamikira

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphero Loyamikira
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pemphelo la Mayamiko
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Ulamulilo wa Yehova Wayamba
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Wamkulu, Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 13

Nyimbo 13

Pemphero Loyamikira

(Salmo 95:2)

1. Yehova ndinu wachisomodi,

Muyeneratu kutamandidwa.

Tigwada kwa inu Womva pemphero,

Kuti inu mutisamalire.

Zolakwa zisonyeza uchimo,

Mutikhululukire machimo.

Munapereka dipo la Yesu.

Tipempha kuti mutiphunzitse.

2. Achimwemwe ndi oitanidwa

Mu bwalo lanu lolangizira.

Mutiphunzitsetu kukudziwani.

Tikonda kukhala m’nyumba yanu.

Dzanja lanu ndi lamphamvu kwambiri,

Lithandiza atumiki anu.

Tikutamanda Ufumu wanu.

Tiulalike, sudzalephera.

3. Tikondwa potisamala bwino,

Anthu onse alambire inu.

Ufumu wanu ndi wabwino zedi,

Udzachotsa matenda ndi imfa.

Mwana wanu adzachotsa zoipa,

Chilengedwe chidzasangalala.

Tiyeni tiimbe mothokoza:

“Titame Yehova Mfumu yathu!”

(Onaninso Sal. 65:2, 4, 11; Afil. 4:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani