LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 106
  • Tikhale pa Ubwenzi ndi Yehova

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tikhale pa Ubwenzi ndi Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kukhala Bwenzi la Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Akupemphani Kuti Mukhale Mnzake
    Na Imwe Mungakhale Mnzake wa Mulungu!
  • Mukhoza Kukhala Bwenzi la Yehova
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Yehova Ndi Bwenzi Lathu Lapamtima
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 106

Nyimbo 106

Tikhale pa Ubwenzi ndi Yehova

(Salimo 15)

1. Ndani angakhale

Bwenzi lanu M’lungu?

Ndani mungakhulupirire,

Angakhale nanu?

Ndi onse amene

Amakukondani,

Amakukhulupirirani,

Okonda cho’nadi.

2. Ndani angakhale

Bwenzi lanu M’lungu?

Ndani angafike

Kumpando wanu wachifumu?

Ndi onse

Amene amakumverani,

Olemekeza dzina lanu,

Okulambirani.

3. Timakuuzani

Zamumtima mwathu,

Ndipo timamva

Kuti tili pafupidi nanu.

Ndi inu tifuna

Kukhala mabwenzi.

Palibiretu bwenzi

Lomwe lingakuposeni.

(Onaninso Sal. 139:1; 1 Pet. 5:6, 7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani