LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 4
  • ‘Yehova ni M’busa Wanga’

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • ‘Yehova ni M’busa Wanga’
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Yehova Ndi M’busa Wanga”
    Imbirani Yehova
  • Kodi Cikondi Cosasintha ca Yehova N’ciani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Tikhale Okhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova
  • Tikhale Okhulupilika Nthawi Zonse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 4

NYIMBO 4

‘Yehova ni M’busa Wanga’

Yopulinta

(Salimo 23)

  1. 1. Yehova ni M’busa wanga,

    Ine nidzam’tsatila.

    Amadziŵa zonse nifuna;

    Amanisamalila.

    Nikakhala na mavuto

    Iye anithandiza.

    Poyenda amanitsogolela,

    Kumalo a mtendele.

    Iye amanitsogolela

    Kumalo a mtendele.

  2. 2. Njila zanu M’busa wanga

    Zimanitsitsimula.

    Conde ine nitetezeni

    Kuti nisasocele.

    Poyenda m’zigwa za mdima,

    Sinidzayopa kanthu.

    Yehova ndinudi Bwenzi langa,

    Ine sinidzayopa.

    Bwenzi langa ndinu Yehova,

    Ine sinidzayopa.

  3. 3. M’lungu ndinu M’busa wanga,

    Nidzakulondolani.

    Inu mumanipatsa mphamvu;

    Mumanilimbikitsa.

    Zonse ndinu munipatsa

    Cifukwa munikonda.

    Sungani moyo wanga Yehova,

    Nimakudalilani.

    Ine nimakudalilani,

    Sungani moyo wanga.

(Onaninso Sal. 28:9; 80:1.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani