LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 33
  • Musawaope!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Musawaope!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Musaŵayope!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 33

Nyimbo 33

Musawaope!

(Mateyo 10:28)

1. Pitanibe anthu anga,

Mulalike uthenga.

Musaope adani.

Anthu onse adziwe

Kuti Mwana wanga Yesu,

Wagwetsadi mdaniyo,

Posachedwa adzam’manga,

Sadzavutitsa anthu.

(KOLASI)

Musaope anthu anga,

Kaya akuopseni.

Ndidzakusamalirani

Monga mwana wa m’diso.

2. Kaya adani n’ngambiri,

Kaya amwetulire

Mwanjira yachinyengo,

Pokusocheretsani.

Musaope anthu anga,

Kaya akuzunzeni,

Ndidzakusamalirani

Mpaka ndiwagonjetsa.

(KOLASI)

Musaope anthu anga,

Kaya akuopseni.

Ndidzakusamalirani

Monga mwana wa m’diso.

3. Sindingakuiwaleni

Ndine Mtetezi wanu.

Ngakhale akupheni,

Ndidzagonjetsa imfa.

Musaope opha thupi

Sangawononge moyo.

Inde, khulupirikani

Mudzalandira mphoto.

(KOLASI)

Musaope anthu anga,

Kaya akuopseni.

Ndidzakusamalirani

Monga mwana wa m’diso.

(Onaninso Deut. 32:10; Neh. 4:14; Sal. 59:1; 83:2, 3.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani