LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 78
  • Phunzitsani Mau a Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Phunzitsani Mau a Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Muzitsimikizira Kuti Zinthu Zofunika Kwambiri Ndi Ziti”
    Imbirani Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Munapeleka Mwana Wanu Wokondeka
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 78

NYIMBO 78

Phunzitsani Mau a Mulungu

Yopulinta

(Machitidwe 18:11)

  1. 1. Timakonda kuphunzitsa

    Anthu za Yehova.

    Madalitso timapeza

    Ni osaneneka.

    Tiphunzitse mwa cikondi

    Monga Yesu Khristu

    Kuti anthu onse

    Ayandikile kwa Yehova.

  2. 2. Tiziyesetsa mwakhama

    Kucita zabwino,

    Kuti onse otiona

    Amvele uthenga.

    Zimene taphunzitsidwa

    Tiphunzitse ena.

    Tidzakhala acimwemwe

    Tikaphunzitsa ena.

  3. 3. M’lungu adzatithandiza

    Pophunzitsa anthu.

    Tikapemphela kwa iye,

    Adzatithandiza.

    Tikonde onse amene

    Tiphunzila nawo.

    Posacedwa nawonso

    Adzapita patsogolo.

(Onaninso Sal. 119:97; 2 Tim. 4:2; Tito 2:7; 1 Yoh. 5:14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani