LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 November tsa. 5
  • “Ndikudziŵa Nchito Zako”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Ndikudziŵa Nchito Zako”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Dongosolo la Mpingo
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Kodi Akulu Amatumikila Mpingo m’Njila Ziti?
    Ndani Amene Akucita Cifunilo Ca Yehova Masiku Ano?
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 November tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | CHIVUMBULUTSO 1–3

“Ndikudziŵa Nchito Zako”

1:20; 2:1, 2

  • Akulu aŵili akukamba na m’bale; Yesu ali na nyenyezi 7 m’dzanja lake

    “Nyenyezi 7”: Akulu odzozedwa komanso akulu onse

  • “M’dzanja [la Yesu] lamanja”: Yesu ndiye ali na mphamvu, ulamulilo na citsogozo pa nyenyezi zimenezo. Ngati wina m’bungwe la akulu afunika kuwongoleledwa, Yesu amaonetsetsa kuti zimenezi zacitika pa nthawi yake komanso m’njila yoyenela

  • “Zoikapo Nyale 7 Zagolide”: Mipingo yacikhristu. Monga mmene coikapo nyale ca m’cihema cinali kuunikila, mipingo yacikhritsu imaunikila coonadi cocokela kwa Mulungu. (Mat. 5:14) Yesu ni “woyenda pakati” pa zoikapo nyale m’njila yakuti, ndiye amayang’anila zocitika za m’mipingo yonse

Kodi masomphenyawa angakuthandizeni bwanji . . .

  • Akulu akakupatsani malangizo kapena uphungu?

  • Mukaona zinthu zopanda cilungamo kapena mavuto mu mpingo mwanu?

  • Kulalikila uthenga wabwino pa mpata uliwonse umene mwapeza?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani