LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 20
  • Munapeleka Mwana Wanu Wokondeka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Munapeleka Mwana Wanu Wokondeka
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Munapeleka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nyimbo Yatsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 20

NYIMBO 20

Munapeleka Mwana Wanu Wokondeka

Yopulinta

(1 Yohane 4:9)

  1. 1. Yehova, Atate,

    Tikuyamikani

    Potuma Yesu

    Kuti atifele.

    Timadzipeleka

    Na mtima umodzi.

    Tidziŵitse ena,

    Cifunilo canu.

    (KOLASI)

    Mwana wanu Yesu,

    Munamupeleka.

    Tidzakutamandani,

    potipatsa Mwana wanu.

  2. 2. Poona cifundo

    Na kukoma mtima,

    Tifuna kukhala

    Mabwenzi anu.

    Yopambana zonse

    Ni mphatso ya Yesu.

    Anadzipeleka

    Cifukwa ca ise.

    KOLASI)

    Mwana wanu Yesu,

    Munamupeleka.

    Tidzakutamandani,

    potipatsa Mwana wanu.

    (KUTSILIZITSA)

    Yehova, Atate, tikuyamikani.

    Cifukwa copeleka Mwana wanu Yesu.

(Onaninso Yoh. 3:16; 15:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani