LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 43
  • Pemphelo la Mayamiko

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphelo la Mayamiko
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pemphero Loyamikira
    Imbirani Yehova
  • “Muziyamika pa Ciliconse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • Tikuyamikani Yehova
    Imbirani Yehova
  • Tikuyamikani Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 43

NYIMBO 43

Pemphelo la Mayamiko

Yopulinta

(Salimo 95:2)

  1. 1. Yehova, Mulungu wamphamvuzonse,

    Tikufikilani mu pemphelo.

    Atate tagwada pamaso panu,

    Conde mvelani pemphelo lathu.

    Nthawi na nthawi ise timacimwa;

    Tipempha mutikhululukile.

    M’namutuma Yesu kudzatifela,

    Tifuna tikutumikileni.

  2. 2. Mulungu wathu tikuyamikila,

    Munatibweletsa m’gulu lanu.

    Tithandizeni, ‘se tiphunzitseni,

    Sitifuna kum’siyani imwe.

    Cifukwa ca mzimu wanu woyela

    Sitimayopa kulalikila.

    Mwacimwemwe tidzakutamandani,

    Ise tidzakutumikilani.

(Onaninso Sal. 65:2, 4, 11; Afil. 4:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani