LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 122
  • Khamu la Abale

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khamu la Abale
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Abale Miyanda Miyanda
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Zoona Zake Ponena za Angelo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawila)—2017
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Aphunzitseni Kucilimika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 122

Nyimbo 122

Khamu la Abale

(Chivumbulutso 7:9, 10)

1. Abale ambirimbiri,

Inde ochuluka,

Aliyense ndi mboni

Yokhulupirika.

Tilipodi ambiri,

Tikuchulukabe.

Tachokeratu ku mafuko

Ndi mitundu yonse.

2. Abale ambirimbiri,

Timalalikira

Uthenga wabwinodi

Kwa ofuna kumva.

Ngakhale tingatope,

Yesu atipatsa

Mpumulo ndi mphamvu zambiri.

Tidzasangalala.

3. Abale ambirimbiri,

Otetezedwadi,

Otumikira M’lungu

Padziko lapansi.

Tilipodi ambiri,

Timalalikira,

Timagwira ntchito ndi

M’lungu Pomutumikira.

(Onaninso Yes. 52:7; Mat. 11:29; Chiv. 7:15.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani