-
1 Mbiri 5:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Ana a Rubeni,+ mwana woyamba wa Isiraeli anali awa: Rubeni anali woyamba kubadwa koma chifukwa chakuti anaipitsa bedi la bambo ake,+ udindo wake monga woyamba kubadwa unaperekedwa kwa ana a Yosefe,+ mwana wa Isiraeli. Choncho iye sanalembedwe monga woyamba kubadwa pamndandanda wa mayina wotsatira makolo.
-