Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 16:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Nthawi yomweyo Aroni anatenga chofukiziracho mogwirizana ndi zimene Mose anamuuza, nʼkuthamanga kukalowa pakati pa mpingowo. Koma mliri unali utayamba kale pakati pawo. Choncho Aroni anaika nsembe yofukiza ija pachofukiziracho nʼkuyamba kuphimbira anthuwo machimo.

  • Numeri 21:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho anthuwo anapita kwa Mose nʼkumuuza kuti: “Tachimwa ife chifukwa cholankhula modandaula potsutsana ndi Yehova ndiponso inuyo.+ Tipepesereni kwa Yehova kuti atichotsere njokazi.” Zitatero Mose anawapepesera kwa Mulungu.+

  • Deuteronomo 9:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Zitatero ndinkadzigwetsa pansi pamaso pa Yehova kwa masiku 40, masana ndi usiku, ngati mmene ndinachitira poyamba. Sindinkadya chakudya kapena kumwa madzi+ chifukwa cha machimo anu onse amene munachita pochita zinthu zoipa pamaso pa Yehova nʼkumukhumudwitsa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani