Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mukawoloka Yorodano+ nʼkukakhala mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti likhale lanu, adzakutetezani kwa adani anu onse okuzungulirani, ndipo mudzakhala otetezeka.+

  • Salimo 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndidzagona pansi mwamtendere nʼkupeza tulo,+

      Chifukwa inu nokha Yehova mumandichititsa kukhala wotetezeka.+

  • Miyambo 1:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Koma munthu wondimvera adzakhala motetezeka+

      Ndipo sadzasokonezeka chifukwa choopa tsoka.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani