- 
	                        
            
            Yoswa 19:49Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        49 Choncho anamaliza kugawa dzikolo ndipo fuko lililonse linali ndi cholowa chake. Kenako Aisiraeli anamʼpatsa Yoswa mwana wa Nuni cholowa chake pakati pawo. 
 
-