Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 36:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iwo anati: “Paja Yehova anakulamulani inu mbuyathu, kuti mugawe dzikoli pochita maere+ kuti likhale cholowa cha Aisiraeli. Yehova anakulamulaninso kuti mupereke cholowa cha mchimwene wathu Tselofekadi kwa ana ake aakazi.+

  • Yoswa 17:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Tselofekadi+ mwana wa Heferi, mwana wa Giliyadi, mwana wa Makiri, mwana wa Manase, analibe ana aamuna, koma aakazi okhaokha. Mayina a anawo anali Mala, Nowa, Hogila, Milika ndi Tiriza. 4 Iwo anapita kwa wansembe Eliezara,+ Yoswa mwana wa Nuni ndi atsogoleri, nʼkuwauza kuti: “Yehova ndi amene analamula Mose kuti atipatse cholowa pakati pa abale athu.”+ Choncho anawapatsa cholowa pakati pa azichimwene a bambo awo, pomvera lamulo la Yehova.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani