- 
	                        
            
            Numeri 15:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        5 Muzikaperekanso vinyo kuti akhale nsembe yachakumwa. Azikakhala wokwana gawo limodzi mwa magawo 4 a muyezo wa hini. Vinyoyo muzikamupereka limodzi ndi nsembe yopsereza,+ kapena ndi nsembe ya mwana wa nkhosa wamphongo. 
 
-