- 
	                        
            
            Levitiko 23:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        21 Pa tsiku limeneli muzilengeza+ kuti kuli msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse yotopetsa. Limeneli ndi lamulo mpaka kalekale kulikonse kumene mungakhale mʼmibadwo yanu yonse. 
 
-