Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 23:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Levitiko 23:34-36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Deuteronomo 16:13-15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nehemiya 8:14-18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno anapeza kuti mʼChilamulo chimene Yehova anawapatsa kudzera mwa Mose analembamo kuti Aisiraeli azikhala mʼmisasa pa nthawi yachikondwerero mʼmwezi wa 7.+ 15 Analembamonso kuti azilengeza mofuula+ mʼmizinda yonse ndi ku Yerusalemu konse kuti: “Pitani kumapiri mukatenge nthambi za mitengo ya maolivi, nthambi za mitengo ya paini, nthambi za mitengo ya mchisu, mitengo ya kanjedza ndi nthambi za masamba ambiri za mitengo ina kuti mudzamangire misasa mogwirizana ndi zimene zinalembedwa.”

      16 Choncho anthu anapita nʼkukatenga zinthu zimenezi ndipo anamangira misasa. Aliyense anamanga msasa pamwamba pa nyumba yake, mʼmabwalo awo, mʼmabwalo a nyumba ya Mulungu woona,+ mʼbwalo lalikulu la Geti la Kumadzi+ ndiponso mʼbwalo lalikulu la Geti la Efuraimu.+ 17 Choncho gulu lonse la anthu amene anabwerera kuchokera ku ukapolo anamanga misasa nʼkukhala mʼmisasayo. Anthu anasangalala kwambiri+ chifukwa Aisiraeli anali asanachitepo zimenezi kuchokera mu nthawi ya Yoswa+ mwana wa Nuni, mpaka nthawi imeneyi. 18 Ndiyeno tsiku lililonse, kuyambira tsiku loyamba mpaka lomaliza, ankawerenga mokweza buku la Chilamulo cha Mulungu woona.+ Anachita chikondwererochi masiku 7 ndipo pa tsiku la 8 anachita msonkhano wapadera mogwirizana ndi Chilamulo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani