- 
	                        
            
            Deuteronomo 17:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        17 “Musamapereke kwa Yehova Mulungu wanu nsembe ya ngʼombe kapena nkhosa imene ili ndi chilema kapena vuto lililonse, chifukwa idzakhala yonyansa kwa Yehova Mulungu wanu.+ 
 
-