- 
	                        
            
            Levitiko 23:36Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        36 Kwa masiku 7 muzipereka nsembe yowotcha pamoto kwa Yehova. Pa tsiku la 8 muzichita msonkhano wopatulika,+ ndipo muzipereka nsembe yowotcha pamoto kwa Yehova. Umenewu ndi msonkhano wapadera. Musamagwire ntchito iliyonse yotopetsa. 
 
-