- 
	                        
            
            Deuteronomo 16:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        16 Mwamuna aliyense pakati panu azikaonekera katatu pa chaka pamaso pa Yehova Mulungu wanu, pamalo amene Mulungu adzasankhe. Azikaonekera pa Chikondwerero cha Mkate Wopanda Zofufumitsa,+ Chikondwerero cha Masabata+ ndi pa Chikondwerero cha Misasa.+ Palibe aliyense wa iwo amene akuyenera kukaonekera kwa Yehova chimanjamanja. 
 
-