- 
	                        
            
            Numeri 19:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        11 Aliyense wokhudza mtembo wa munthu aliyense, azikhala wodetsedwa kwa masiku 7.+ 
 
- 
                                        
- 
	                        
            
            Numeri 19:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        16 Aliyense amene wakhudza munthu amene waphedwa ndi lupanga kunja kwa msasa, kapena mtembo, fupa la munthu, kapenanso manda, adzakhala wodetsedwa kwa masiku 7.+ 
 
-