- 
	                        
            
            Numeri 19:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        20 Koma munthu wodetsedwa akapanda kudziyeretsa, aziphedwa kuti asakhalenso mumpingowo,+ chifukwa wadetsa malo opatulika a Yehova. Iye sanawazidwe madzi oyeretsera, choncho ndi wodetsedwa. 
 
-