Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 14:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ana anu adzakhala abusa mʼchipululu kwa zaka 40,+ ndipo adzavutika chifukwa cha kusakhulupirika kwanu,* mpaka womalizira kufa wa inu atagona mʼmanda mʼchipululu muno.+

  • Deuteronomo 29:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yoswa 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Aisiraeliwo anayenda mʼchipululu zaka 40,+ mpaka anthu onse amene anatuluka mu Iguputo, amene sanamvere mawu a Yehova+ atatha kuphatikizapo amuna onse otha kupita kunkhondo. Amenewo Yehova anawalumbirira kuti sadzawalola kuona dziko+ limene Yehova analumbirira makolo awo kuti adzalipereka kwa anthu ake,*+ dziko loyenda mkaka ndi uchi.+

  • Salimo 95:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kwa zaka 40, mʼbadwo umenewo unkandinyansa ndipo ndinati:

      “Awa ndi anthu amene mitima yawo imasochera nthawi zonse,

      Njira zanga sakuzidziwa.”

  • Machitidwe 13:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani