- 
	                        
            
            Deuteronomo 4:38Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        38 Anachotsa pamaso panu mitundu yaikulu ndi yamphamvu kuposa inu, kuti akulowetseni mʼdziko lawo nʼkukupatsani kuti likhale cholowa chanu ngati mmene zilili lero.+ 
 
- 
                                        
- 
	                        
            
            Yoswa 14:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        14 Aisiraeli anatenga cholowa chawo mʼdziko la Kanani. Wansembe Eliezara, Yoswa mwana wa Nuni ndi atsogoleri a mafuko a makolo a Aisiraeli ndi amene anawagawira cholowachi.+ 
 
-