- 
	                        
            
            Numeri 3:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        32 Mkulu wa atsogoleri onse a Alevi anali Eleazara,+ mwana wa wansembe Aroni. Iye ndi amene ankayangʼanira anthu onse amene ankatumikira pamalo oyera. 
 
- 
                                        
- 
	                        
            
            Yoswa 14:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        14 Aisiraeli anatenga cholowa chawo mʼdziko la Kanani. Wansembe Eliezara, Yoswa mwana wa Nuni ndi atsogoleri a mafuko a makolo a Aisiraeli ndi amene anawagawira cholowachi.+ 
 
-