- 
	                        
            
            Numeri 36:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        6 Zimene Yehova walamula zokhudza ana aakazi a Tselofekadi nʼzakuti: ‘Iwo angakwatiwe ndi aliyense amene angamukonde. Koma ayenera kukwatiwa ndi amuna a fuko la makolo awo okha. 
 
-