- 
	                        
            
            Levitiko 7:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        7 Lamulo la nsembe yakupalamula ndi lofanana ndi la nsembe yamachimo. Nyama ya nsembeyi izikhala ya wansembe amene wapereka nsembeyo pophimba machimo.+ 
 
-