- 
	                        
            
            Numeri 8:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        7 Kuti uwayeretse uchite izi: Uwawaze madzi oyeretsera machimo ndipo iwo amete thupi lonse ndi lezala. Komanso achape zovala zawo nʼkudziyeretsa.+ 
 
-