- 
	                        
            
            2 Samueli 10:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        6 Patapita nthawi, Aamoni anaona kuti akhala ngati chinthu chonunkha kwa Davide. Choncho anatumiza anthu kuti akalembe ganyu Asiriya a ku Beti-rehobu+ ndi Asiriya a ku Zoba+ ndipo onse pamodzi analipo asilikali 20,000 oyenda pansi. Anapitanso kwa mfumu ya ku Maaka+ nʼkulemba ganyu amuna 1,000 komanso ku Isitobu amuna 12,000.+ 
 
- 
                                        
- 
	                        
            
            2 Samueli 10:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        8 Ndiyeno Aamoni anapita kukaima pageti la mzinda atakonzekera kumenya nkhondo. Pomwe Asiriya a ku Zoba, a ku Rehobu, a ku Isitobu ndi a ku Maaka anakayalana kwaokha kutchire. 
 
-