Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 7:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mukaganiza mumtima mwanu kuti, ‘Anthu a mitundu iyi ndi ambiri kuposa ife. Tingathe bwanji kuwathamangitsa?’+ 18 musawaope.+ Nthawi zonse muzikumbukira zimene Yehova Mulungu wanu anachitira Farao ndi Iguputo yense.+

  • Deuteronomo 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iye aziwauza kuti, ‘Tamverani Aisiraeli inu. Mwatsala pangʼono kumenyana ndi adani anu. Mitima yanu isachite mantha. Musaope, kuchita mantha kapena kunjenjemera chifukwa cha iwo,

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani