Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 21:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mfumu ya Akanani ya ku Aradi+ yomwe inkakhala ku Negebu itamva kuti Aisiraeli akubwera kudzera njira ya ku Atarimu, inapita kukamenyana nawo ndipo inagwira Aisiraeli ena nʼkupita nawo kudziko lake.

  • Numeri 21:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho Yehova anamva mawu a Aisiraeli ndipo anapereka Akananiwo mʼmanja mwawo. Aisiraeli anawononga Akananiwo limodzi ndi mizinda yawo. Nʼchifukwa chake malowo anawatchula kuti Horima.*+

  • Deuteronomo 1:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Kenako Aamori amene ankakhala mʼphirimo anatuluka kudzakumana nanu ndipo anakuthamangitsani ngati mmene njuchi zimachitira, moti anakubalalitsani ku Seiri mpaka kukafika ku Horima.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani