- 
	                        
            
            Levitiko 27:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        27 Koma ngati ndi nyama yodetsedwa ndipo waiwombola mogwirizana ndi mtengo womwe unaikidwa, azipereka mtengo wa nyamayo nʼkuwonjezerapo limodzi mwa magawo 5 a mtengowo.+ Koma ngati sangaiwombole izigulitsidwa pa mtengo womwe unaikidwa. 
 
-