Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 15:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Numeri 26:59
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Mkazi wa Amuramu anali Yokebedi,+ mwana wa Levi. Mkazi wa Levi anamuberekera mwana ameneyu ku Iguputo. Yokebedi anaberekera Amuramu ana awa: Aroni, Mose ndi mchemwali wawo Miriamu.+

  • Mika 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ine ndinakutulutsani mʼdziko la Iguputo,+

      Ndinakuwombolani mʼnyumba ya ukapolo,+

      Ndipo ndinakutumizirani Mose, Aroni ndi Miriamu kuti akutsogolereni.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani