- 
	                        
            
            Numeri 22:16, 17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        16 Iwo anapita kwa Balamu nʼkukamuuza kuti: “Balaki mwana wa Zipori wanena kuti, ‘Musalole kuti china chilichonse chikulepheretseni kubwera kwa ine, 17 chifukwa ndidzakupatsani mphoto yaikulu, ndipo ndidzachita chilichonse chimene mungandiuze. Chonde tabwerani mudzatemberere anthuwa.’” 
 
-