Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Numeri 25:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Dzina la mwamuna wa Chiisiraeli, amene anaphedwa limodzi ndi mkazi wa Chimidiyani uja linali Zimiri mwana wa Salu, ndipo anali mtsogoleri wa nyumba ya makolo a fuko la Simiyoni. 15 Dzina la mkazi wa Chimidiyani amene anaphedwayo linali Kozibi, mwana wa Zuri.+ Zuri anali mtsogoleri wa fuko la nyumba ina ya makolo ku Midiyani.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani