Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 4:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Anthu ochokera mʼmitundu yonse ankabwera kudzamva nzeru za Solomo, ngakhalenso mafumu onse apadziko lapansi amene anamva za nzeru zake.+

  • 1 Mafumu 10:4-7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Danieli 1:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mfumuyo italankhula nawo, inaona kuti pagulu lonselo panalibe aliyense amene ankafanana ndi Danieli, Hananiya, Misayeli ndi Azariya.+ Choncho anyamata amenewa anapitiriza kutumikira mfumu. 20 Pa nkhani iliyonse yofunika nzeru komanso kuzindikira, imene mfumu inkawafunsa, inaona kuti iwo anali anzeru kuwirikiza maulendo 10 kuposa ansembe onse ochita zamatsenga ndi anthu onse olankhula ndi mizimu+ amene anali mu ufumu wake wonse.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani