Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Levitiko 11:13-20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Izi ndi zamoyo zouluka zimene muyenera kuziona kuti ndi zonyansa. Sizikuyenera kudyedwa chifukwa ndi zonyansa: chiwombankhanga,+ nkhwazi, muimba wakuda,+ 14 mphamba wofiira, mtundu uliwonse wa mphamba wakuda, 15 mtundu uliwonse wa khwangwala, 16 nthiwatiwa, kadzidzi, kakowa, mtundu uliwonse wa kabawi, 17 nkhwezule, chiswankhono, mantchichi, 18 tsekwe, vuwo, muimba, 19 dokowe, mtundu uliwonse wa chimeza, sadzu ndi mleme. 20 Tizilombo tonse timene timapezeka tambiri, tamapiko ndiponso tamiyendo 4, ndi tonyansa kwa inu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani