Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 15:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pakati panu pasapezeke munthu wosauka, chifukwa Yehova adzakudalitsani ndithu+ mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti likhale cholowa chanu.

  • Deuteronomo 15:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ngati mmodzi mwa abale anu wasauka pakati panu, mu umodzi mwa mizinda yanu mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, musamamuumire mtima kapena kumuumitsira dzanja lanu.+

  • Deuteronomo 15:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Muzimupatsa mowolowa manja zimene akufunazo,+ ndipo musamamupatse* zinthuzo monyinyirika. Mukamachita zimenezi, Yehova Mulungu wanu adzakudalitsani pa chilichonse chimene mukuchita ndi ntchito zanu zonse.+

  • Miyambo 19:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Luka 6:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani