Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Oweruza 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Apa nʼkuti anthu atabisalira Samisoni mʼchipinda china. Mkaziyo anamuuza kuti: “Afilisiti aja abwera Samisoni!” Atamva zimenezo, Samisoni anadula zingwe zija ngati mmene ulusi* umadukira ukagwira moto.+ Chinsinsi cha mphamvu zake sichinadziwike.

  • Oweruza 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno Delila anatenga zingwe zatsopano nʼkumumanga nazo manja ndipo anamuuza kuti: “Afilisiti aja abwera Samisoni!” (Pa nthawiyi nʼkuti anthu atamʼbisalira mʼchipinda china.) Samisoni atamva zimenezi anadula zingwe zimene anamʼmanga nazozo ngati akudula ulusi.+

  • Oweruza 16:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iye anamangadi zingongozo nʼkuzipina. Kenako anamuuza kuti: “Afilisiti aja abwera Samisoni!” Samisoni atamva zimenezi anadzuka ndipo anachotsa chopinira chija komanso ulusi uja.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani