Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 15:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Deuteronomo 4:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Inuyo mwasonyezedwa zinthu zimenezi kuti mudziwe kuti Yehova ndi Mulungu woona.+ Palibenso Mulungu wina kupatulapo iyeyo.+

  • Salimo 73:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 86:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu Yehova, palibe mulungu wina amene angafanane ndi inu,+

      Palibe aliyense amene wachita zinthu zofanana ndi zimene inu mwachita.+

  • Salimo 89:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndi ndani kumwamba amene angafanane ndi Yehova?+

      Ndi ndani pakati pa ana a Mulungu+ amene ndi wofanana ndi Yehova?

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani